News from Malawi
Stay current with all the latest and breaking news about Malawi, compare headlines and perspectives between news sources on stories happening today. In total, 2,632 stories have been published about Malawi which Ground News has aggregated in the past 3 months.
Local News Publishers
Suggest a source
Looking for a source we don't already have? Suggest one here.Top Malawi News
Latest News Stories
Malawi · MalawiZadziwika kuti ophunzira ambiri a mu sukulu za ukachenjede chingerezi chikumawapeta ndipo ambiri sakwanitsa kufotokoza komanso kulemba m’chizungu chomveka bwino. Izi ndi malingana ndi otsatira kwa wachiwiri wa Chancellor ku sukulu ya ukachenjede ya University of Malawi (UNIMA), Dr Sunduzwayo Madise yemwe wati kusowa kwa ukadaulo pa kaphunzitsidwe kamakono maka kuyambira ku m’mela mpoyamba kukuwonjezera kuvutika […] The post Chizungu chikucheka …See the Story
Chizungu chikucheka ma galajuweti amene - atero a UNIMA Malawi 24 | Latest News from Malawi
Malawi · MalawiThe Centre for Democracy and Economic Development Initiatives (CDEDI) has urged the Tonse Government and President Dr. Lazarus Chakwera to rise above party politics and stop from dipping its fingers in the public to finance Malawi Congress Party (MCP) campaign rallies a head of the 2025 General Election. CDEDI Executive Director Sylvester Namiwa spoke during […]
The post Namiwa’s CDEDI wants Govt to pay back funds used for Kamuzu Day celebration…See the Story
Namiwa’s CDEDI wants Govt to pay back funds used for Kamuzu Day celebrations, Kunkuyu says all holiday celebrations have costs
Malawi · MalawiInu amene mukumapeza mwayi otsukuluza mkamwa pa nkhani zokhudza mtsogoleri wa dziko lino a Chakwera yambani kuyenda mosamala. Ayamba kunjata anthu kunja kuno ati chifukwa chonyoza a Chakwera. A Sainani Nkhoma a ku Dowa akuyembekezeka kumva chigamulo chawo sabata la mawa pamene a bwalo apeza kuti mkuluyu anatsukuluza mkamwa pothilira ndemanga pa nkhani yokhudza a […] The post Watsekeledwa wina chifukwa chonyoza Chakwera pa WhatsApp appeared first…See the Story
Watsekeledwa wina chifukwa chonyoza Chakwera pa WhatsApp Malawi 24 | Latest News from Malawi
Malawi · MalawiIt never rains but pour for South African government in the ongoing extradition case involving Prophet Shepherd Bushiri and wife, Mary, as the Chief Resident Magistrate Court has rejected their application to have the defense change the questioning techniques used in the cross examination. On Tuesday, during cross examining South Africa’s only witness, Sibongile Mnzinyathi […]
The post South Africa suffers a fresh blow in Bushiri case as court r…See the Story
South Africa suffers a fresh blow in Bushiri case as court reject protection of witness from being grilled
Malawi · MalawiBy Chisomo Phiri The Parliamentary Committee on Government Assurance and Public Sector Reforms has expressed satisfaction with the progress of the Social Cash Transfer Program in Balaka District. The committee’s…See the Story
Parliamentary Committee applauds social cash transfer program's impact in Balaka district
Peter Mutharika · MalawiMtsogoleri wa dziko lino Lazarus Chakwera wati sibwino kunamiza aMalawi kuti dziko likhonza kumangidwa popanda maziko ovuta komanso a misozi, ndipo kulankhula motha mawu otere ndi chifukwa choti omwe adali m’boma m’mbuyomu adaba ndipo palibe akuwalondola nde akuwona kuti nzophweka kungomanga dziko mwachidule. Polankhula pa mwambo okhazikitsa zipangizo za makono za ulimi ku BICC mu […] The post Musandilankhulitse Pambali – Chakwera appeared f…See the Story